×

Ndi pamene iwe udasiya abale ako m’mawa kukayika anthu okhulupirira ku malo 3:121 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:121) ayat 121 in Chichewa

3:121 Surah al-‘Imran ayat 121 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 121 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَإِذۡ غَدَوۡتَ مِنۡ أَهۡلِكَ تُبَوِّئُ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ مَقَٰعِدَ لِلۡقِتَالِۗ وَٱللَّهُ سَمِيعٌ عَلِيمٌ ﴾
[آل عِمران: 121]

Ndi pamene iwe udasiya abale ako m’mawa kukayika anthu okhulupirira ku malo omenyera nkhondo. Mulungu ndi wakumva ndi wodziwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ غدوت من أهلك تبوئ المؤمنين مقاعد للقتال والله سميع عليم, باللغة نيانجا

﴿وإذ غدوت من أهلك تبوئ المؤمنين مقاعد للقتال والله سميع عليم﴾ [آل عِمران: 121]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukira) pamene unachoka m’mawa kusiya banja lako kuti uwakonzere Asilamu malo omenyanira (nkhondo). Ndipo Allah Ngwakumva, Ngodziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek