×

Pamene magulu anu awiri adali ndi mantha koma Mulungu adali Mtetezi wawo. 3:122 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:122) ayat 122 in Chichewa

3:122 Surah al-‘Imran ayat 122 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 122 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿إِذۡ هَمَّت طَّآئِفَتَانِ مِنكُمۡ أَن تَفۡشَلَا وَٱللَّهُ وَلِيُّهُمَاۗ وَعَلَى ٱللَّهِ فَلۡيَتَوَكَّلِ ٱلۡمُؤۡمِنُونَ ﴾
[آل عِمران: 122]

Pamene magulu anu awiri adali ndi mantha koma Mulungu adali Mtetezi wawo. Ndipo mwa Mulungu anthu okhulupirira ayenera kuika chikhulupiliro chawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ همت طائفتان منكم أن تفشلا والله وليهما وعلى الله فليتوكل المؤمنون, باللغة نيانجا

﴿إذ همت طائفتان منكم أن تفشلا والله وليهما وعلى الله فليتوكل المؤمنون﴾ [آل عِمران: 122]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukira) pamene magulu awiri mwa inu anafunitsitsa kuti athawe (chifukwa cha mantha monga momwe adathawira achinyengo). Koma Allah adali Mtetezi wa magulu awiriwo. (Choncho adawasunga kuti asathawe). Ndipo okhulupirira ayadzamire kwa Allah Yekha basi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek