×

Muhammad siwina aliyense koma Mtumwi ndipo, ndithudi, Atumwi ena adalipo kale iye 3:144 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:144) ayat 144 in Chichewa

3:144 Surah al-‘Imran ayat 144 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 144 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَمَا مُحَمَّدٌ إِلَّا رَسُولٞ قَدۡ خَلَتۡ مِن قَبۡلِهِ ٱلرُّسُلُۚ أَفَإِيْن مَّاتَ أَوۡ قُتِلَ ٱنقَلَبۡتُمۡ عَلَىٰٓ أَعۡقَٰبِكُمۡۚ وَمَن يَنقَلِبۡ عَلَىٰ عَقِبَيۡهِ فَلَن يَضُرَّ ٱللَّهَ شَيۡـٔٗاۚ وَسَيَجۡزِي ٱللَّهُ ٱلشَّٰكِرِينَ ﴾
[آل عِمران: 144]

Muhammad siwina aliyense koma Mtumwi ndipo, ndithudi, Atumwi ena adalipo kale iye asanadze. Ngati iye akufa kapena aphedwa, kodi inu mudzabwerera m’mbuyo? Yense amene abwerera m’mbuyo sadzachita chilichonse chopweteka Mulungu ndipo Mulungu adzalipira anthu oyamika

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما محمد إلا رسول قد خلت من قبله الرسل أفإن مات أو, باللغة نيانجا

﴿وما محمد إلا رسول قد خلت من قبله الرسل أفإن مات أو﴾ [آل عِمران: 144]

Khaled Ibrahim Betala
“Muhammad (s.a.w) sali chinthu china koma Mtumiki chabe. Patsogolo pake adamuka atumiki ambiri. Kodi ngati atamwalira kapena kuphedwa, mungabwelerenso m’mbuyo? Ndipo amene abwelere m’mbuyo mwake savutitsa Allah ndi chilichonse; koma Allah adzalipira othokoza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek