×

Ndipo palibe amene amafa kupatula ndi chilolezo cha Mulungu ndi pa nthawi 3:145 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:145) ayat 145 in Chichewa

3:145 Surah al-‘Imran ayat 145 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 145 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَمَا كَانَ لِنَفۡسٍ أَن تَمُوتَ إِلَّا بِإِذۡنِ ٱللَّهِ كِتَٰبٗا مُّؤَجَّلٗاۗ وَمَن يُرِدۡ ثَوَابَ ٱلدُّنۡيَا نُؤۡتِهِۦ مِنۡهَا وَمَن يُرِدۡ ثَوَابَ ٱلۡأٓخِرَةِ نُؤۡتِهِۦ مِنۡهَاۚ وَسَنَجۡزِي ٱلشَّٰكِرِينَ ﴾
[آل عِمران: 145]

Ndipo palibe amene amafa kupatula ndi chilolezo cha Mulungu ndi pa nthawi yokhazikitsidwa kale. Ndipo iye amene afuna malipiro a m’dziko lino, Ife tidzamupatsa ndipo iye amene afuna malipiro a m’moyo umene uli nkudza Ife tidzamupatsa. Ndipo Ife tidzalipira anthu othokoza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان لنفس أن تموت إلا بإذن الله كتابا مؤجلا ومن يرد, باللغة نيانجا

﴿وما كان لنفس أن تموت إلا بإذن الله كتابا مؤجلا ومن يرد﴾ [آل عِمران: 145]

Khaled Ibrahim Betala
“Munthu aliyense sangafe pokhapokha mwa chilolezo cha Allah, (ndi kukwanira) nthawi yake yolembedwa. Ndipo amene akufuna mphoto ya pa dziko la pansi, timpatsa pompo; ndipo amene akufuna Mphoto ya tsiku lachimaliziro tidzampatsa konko. Ndipo, tidzawalipira (zabwino) othokoza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek