×

oh inu anthu okhulupirira! Musakhale ngati osakhulupirira amene amanena kwa abale awo 3:156 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:156) ayat 156 in Chichewa

3:156 Surah al-‘Imran ayat 156 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 156 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ لَا تَكُونُواْ كَٱلَّذِينَ كَفَرُواْ وَقَالُواْ لِإِخۡوَٰنِهِمۡ إِذَا ضَرَبُواْ فِي ٱلۡأَرۡضِ أَوۡ كَانُواْ غُزّٗى لَّوۡ كَانُواْ عِندَنَا مَا مَاتُواْ وَمَا قُتِلُواْ لِيَجۡعَلَ ٱللَّهُ ذَٰلِكَ حَسۡرَةٗ فِي قُلُوبِهِمۡۗ وَٱللَّهُ يُحۡيِۦ وَيُمِيتُۗ وَٱللَّهُ بِمَا تَعۡمَلُونَ بَصِيرٞ ﴾
[آل عِمران: 156]

oh inu anthu okhulupirira! Musakhale ngati osakhulupirira amene amanena kwa abale awo pamene ayenda padziko kapena apita kunkhondo: “Akadakhala kuti adali ndi ife kuno, iwo sakadafa ayi kapena sakadaphedwa.” Mulungu amatero kuti iwo adzakumbukire mawu awo. Ndi Mulunguameneamaperekamoyondiimfa. Ndipo Mulungu amaona ntchito zonse zimene mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا لا تكونوا كالذين كفروا وقالوا لإخوانهم إذا ضربوا في, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا لا تكونوا كالذين كفروا وقالوا لإخوانهم إذا ضربوا في﴾ [آل عِمران: 156]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Musakhale ngati amene sadakhulupirire, nanena za anzawo pamene akuyenda pa dziko kapena pomwe akumenyana nkhondo (ndikufera konko): “Akadakhala ndi ife sakadafa, ndiponso sakadaphedwa.” Allah (adawathira maganizo amenewa) kuti azipange zimenezo kukhala zodandaulitsa m’mitima mwawo. Komatu Allah ndi amene amapereka moyo ndi imfa. Ndipo Allah akuona zonse zomwe mukuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek