×

Ena a inu amene mudathawa patsiku limene anthu a magulu awiri ankhondo 3:155 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:155) ayat 155 in Chichewa

3:155 Surah al-‘Imran ayat 155 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 155 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ تَوَلَّوۡاْ مِنكُمۡ يَوۡمَ ٱلۡتَقَى ٱلۡجَمۡعَانِ إِنَّمَا ٱسۡتَزَلَّهُمُ ٱلشَّيۡطَٰنُ بِبَعۡضِ مَا كَسَبُواْۖ وَلَقَدۡ عَفَا ٱللَّهُ عَنۡهُمۡۗ إِنَّ ٱللَّهَ غَفُورٌ حَلِيمٞ ﴾
[آل عِمران: 155]

Ena a inu amene mudathawa patsiku limene anthu a magulu awiri ankhondo adakumana, ndi Satana amene adawapangitsa kuti athawe zimene adachita. Zoonadi Mulungu adawakhululukira. Ndithudi Mulungu ndi okhululukira ndi wopilira kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين تولوا منكم يوم التقى الجمعان إنما استزلهم الشيطان ببعض ما, باللغة نيانجا

﴿إن الذين تولوا منكم يوم التقى الجمعان إنما استزلهم الشيطان ببعض ما﴾ [آل عِمران: 155]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi, mwa inu amene adabwerera m’mbuyo (kuthawa) tsiku lomwe magulu awiri a nkhondo adakumana (pa nkhondo ya Uhudi; gulu la osakhulupirira ndi gulu lankhondo la Asilamu), satana ndiyemwe adawaterezetsa chifukwa cha zina (zolakwa) zomwe adachita; ndipo Allah (tsopano) wawakhululukira. Ndithudi, Allah Ngokhululuka kwambiri, Ngoleza koposa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek