×

Ndipo ngati inu muphedwa kapena mukufa mnjira ya Mulungu, chikhululukiro ndi chifundo 3:157 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:157) ayat 157 in Chichewa

3:157 Surah al-‘Imran ayat 157 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 157 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿وَلَئِن قُتِلۡتُمۡ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِ أَوۡ مُتُّمۡ لَمَغۡفِرَةٞ مِّنَ ٱللَّهِ وَرَحۡمَةٌ خَيۡرٞ مِّمَّا يَجۡمَعُونَ ﴾
[آل عِمران: 157]

Ndipo ngati inu muphedwa kapena mukufa mnjira ya Mulungu, chikhululukiro ndi chifundo chochokera kwa Mulungu ndi chabwino kuposa chuma chimene akusonkhanitsa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولئن قتلتم في سبيل الله أو متم لمغفرة من الله ورحمة خير, باللغة نيانجا

﴿ولئن قتلتم في سبيل الله أو متم لمغفرة من الله ورحمة خير﴾ [آل عِمران: 157]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ngati mwaphedwa pa njira ya Allah, kapena kufa, (palibe chotaika kwa inu) pakuti chikhululuko ndi chisoni zochokera kwa Allah nzabwino kuposa zomwe akuzisonkhanitsa (pa moyo wa pa dziko lapansi)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek