×

Pamene mavuto adza pa inu ngakhale kuti inu mudapha anthu kwambiri, inu 3:165 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:165) ayat 165 in Chichewa

3:165 Surah al-‘Imran ayat 165 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 165 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿أَوَلَمَّآ أَصَٰبَتۡكُم مُّصِيبَةٞ قَدۡ أَصَبۡتُم مِّثۡلَيۡهَا قُلۡتُمۡ أَنَّىٰ هَٰذَاۖ قُلۡ هُوَ مِنۡ عِندِ أَنفُسِكُمۡۗ إِنَّ ٱللَّهَ عَلَىٰ كُلِّ شَيۡءٖ قَدِيرٞ ﴾
[آل عِمران: 165]

Pamene mavuto adza pa inu ngakhale kuti inu mudapha anthu kwambiri, inu mudati: “Kodi zichokera kuti izi?” Nena: “Zimenezi zichokera kwa inu nomwe. Ndithudi Mulungu ali ndi mphamvu pa chinthu china chilichonse.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أو لما أصابتكم مصيبة قد أصبتم مثليها قلتم أنى هذا قل هو, باللغة نيانجا

﴿أو لما أصابتكم مصيبة قد أصبتم مثليها قلتم أنى هذا قل هو﴾ [آل عِمران: 165]

Khaled Ibrahim Betala
“Pamene sautso lidakupezani lomwe inu mudawathira nalo (adani anu) lochulukirapo kawiri, mudanena: “Lachokera kuti (sautso) ili?” Nena: “Ilo lachokera kwa inu eni (chifukwa cha kunyoza lamulo lomwe adakuuzani). Ndithudi, Allah Ngokhoza chilichonse.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek