×

Ndithudi Mulungu wamva mawu a iwo amene adati: “Ndithudi Mulungu ndi osauka 3:181 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:181) ayat 181 in Chichewa

3:181 Surah al-‘Imran ayat 181 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 181 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿لَّقَدۡ سَمِعَ ٱللَّهُ قَوۡلَ ٱلَّذِينَ قَالُوٓاْ إِنَّ ٱللَّهَ فَقِيرٞ وَنَحۡنُ أَغۡنِيَآءُۘ سَنَكۡتُبُ مَا قَالُواْ وَقَتۡلَهُمُ ٱلۡأَنۢبِيَآءَ بِغَيۡرِ حَقّٖ وَنَقُولُ ذُوقُواْ عَذَابَ ٱلۡحَرِيقِ ﴾
[آل عِمران: 181]

Ndithudi Mulungu wamva mawu a iwo amene adati: “Ndithudi Mulungu ndi osauka koma ife ndife olemera.” Ife tidzalemba zomwe amanena ndi kupha kwawo kwa Atumwi opanda chifukwa ndipo Ife tidzanena kuti: “Lawani chilango chanu cha moto wowotcha.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لقد سمع الله قول الذين قالوا إن الله فقير ونحن أغنياء سنكتب, باللغة نيانجا

﴿لقد سمع الله قول الذين قالوا إن الله فقير ونحن أغنياء سنكتب﴾ [آل عِمران: 181]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu Allah wamva liwu (lonyogodola) la omwe (Ayuda) anena kuti: “Allah ngosauka, ndipo ife ndife olemera.” Tazilemba zimene anena, ndipo (talembanso) kupha kwawo aneneri popanda choonadi. Ndipo tidzawauza (tsiku la chiweruziro): “Lawani chilango cha Moto owotcha.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek