×

Musaganize kuti iwo amene amasangalala ndi zimene achita ndiponso iwo amene amafuna 3:188 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:188) ayat 188 in Chichewa

3:188 Surah al-‘Imran ayat 188 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 188 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿لَا تَحۡسَبَنَّ ٱلَّذِينَ يَفۡرَحُونَ بِمَآ أَتَواْ وَّيُحِبُّونَ أَن يُحۡمَدُواْ بِمَا لَمۡ يَفۡعَلُواْ فَلَا تَحۡسَبَنَّهُم بِمَفَازَةٖ مِّنَ ٱلۡعَذَابِۖ وَلَهُمۡ عَذَابٌ أَلِيمٞ ﴾
[آل عِمران: 188]

Musaganize kuti iwo amene amasangalala ndi zimene achita ndiponso iwo amene amafuna kuyamikidwa pa zinthu zimene iwo sanachite, kuti adzathawa chilango chathu, ndipo chilango chowawa chiri kuwadikira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لا تحسبن الذين يفرحون بما أتوا ويحبون أن يحمدوا بما لم يفعلوا, باللغة نيانجا

﴿لا تحسبن الذين يفرحون بما أتوا ويحبون أن يحمدوا بما لم يفعلوا﴾ [آل عِمران: 188]

Khaled Ibrahim Betala
“Musaganize kuti amene akukondwera ndi zinthu (zoipa) zomwe achita nakonda kutamandidwa ndi zomwe sadachite, musawaganizire kuti akapulumuka. (Koma kuti) pa iwo padzakhala chilango chopweteka
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek