×

“Ambuye wathu! Ndithudi ife tamva kuitana kwa iye amene ali kuwaitana anthu 3:193 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:193) ayat 193 in Chichewa

3:193 Surah al-‘Imran ayat 193 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 193 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿رَّبَّنَآ إِنَّنَا سَمِعۡنَا مُنَادِيٗا يُنَادِي لِلۡإِيمَٰنِ أَنۡ ءَامِنُواْ بِرَبِّكُمۡ فَـَٔامَنَّاۚ رَبَّنَا فَٱغۡفِرۡ لَنَا ذُنُوبَنَا وَكَفِّرۡ عَنَّا سَيِّـَٔاتِنَا وَتَوَفَّنَا مَعَ ٱلۡأَبۡرَارِ ﴾
[آل عِمران: 193]

“Ambuye wathu! Ndithudi ife tamva kuitana kwa iye amene ali kuwaitana anthu kuti adze ku chipembedzo choonadi.” Iye adati: “Khulupirirani mwa Ambuye wanu ndipo ife takhulupirira. Ambuye wathu tikhululukireni ife machimo athu ndipo chotsani kwa ife ntchito zathu zoipa ndipo tipangeni kuti tife pamodzi ndi anthu olungama.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ربنا إننا سمعنا مناديا ينادي للإيمان أن آمنوا بربكم فآمنا ربنا فاغفر, باللغة نيانجا

﴿ربنا إننا سمعنا مناديا ينادي للإيمان أن آمنوا بربكم فآمنا ربنا فاغفر﴾ [آل عِمران: 193]

Khaled Ibrahim Betala
““E Mbuye wathu! Ndithudi, ife tamva woitana akuitanira ku chikhulupiliro kuti: ‘Khulupirirani Mbuye wanu,’ ndipo takhulupirira. E Mbuye wathu! Tikhululukireni machimo athu ndi kutifafanizira zoipa zathu, ndipo mutenge mizimu yathu tili pamodzi ndi anthu abwino.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek