×

Kale ngati ulangizi kwa anthu ndipo adatumiza muyeso. Ndithudi iwo amene amakana 3:4 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:4) ayat 4 in Chichewa

3:4 Surah al-‘Imran ayat 4 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 4 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿مِن قَبۡلُ هُدٗى لِّلنَّاسِ وَأَنزَلَ ٱلۡفُرۡقَانَۗ إِنَّ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ بِـَٔايَٰتِ ٱللَّهِ لَهُمۡ عَذَابٞ شَدِيدٞۗ وَٱللَّهُ عَزِيزٞ ذُو ٱنتِقَامٍ ﴾
[آل عِمران: 4]

Kale ngati ulangizi kwa anthu ndipo adatumiza muyeso. Ndithudi iwo amene amakana chivumbulutso cha Mulungu adzalangidwa kwambiri. Ndipo Mulungu ndi wamphamvu ndiponso Mwini kubwezera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: من قبل هدى للناس وأنـزل الفرقان إن الذين كفروا بآيات الله لهم, باللغة نيانجا

﴿من قبل هدى للناس وأنـزل الفرقان إن الذين كفروا بآيات الله لهم﴾ [آل عِمران: 4]

Khaled Ibrahim Betala
“Kale, kuti (mabukuwo) akhale chotsogolera anthu. Ndipo adavumbulutsa (Qur’an) yolekanitsa pakati pa choonadi ndi chonama * Ndithudi, aja amene sadakhulupirire zizindikiro za Allah, adzakhala ndi chilango chaukali. Ndipo Allah Ngwamphamvu zoposa, Wobwezera (chilango mwaukali)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek