×

Iye ndiye amene amakukonzani pamene muli m’mimba mwa amayi anu mwa chifuniro 3:6 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:6) ayat 6 in Chichewa

3:6 Surah al-‘Imran ayat 6 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 6 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿هُوَ ٱلَّذِي يُصَوِّرُكُمۡ فِي ٱلۡأَرۡحَامِ كَيۡفَ يَشَآءُۚ لَآ إِلَٰهَ إِلَّا هُوَ ٱلۡعَزِيزُ ٱلۡحَكِيمُ ﴾
[آل عِمران: 6]

Iye ndiye amene amakukonzani pamene muli m’mimba mwa amayi anu mwa chifuniro chake. Kulibe Mulungu wina koma Iye yekha, Mwini mphamvu ndi Mwini nzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: هو الذي يصوركم في الأرحام كيف يشاء لا إله إلا هو العزيز, باللغة نيانجا

﴿هو الذي يصوركم في الأرحام كيف يشاء لا إله إلا هو العزيز﴾ [آل عِمران: 6]

Khaled Ibrahim Betala
“Iye ndi Yemwe amakulinganizani muli m’mimba mmaonekedwe anu mmene akufunira. Palibe wopembedzedwa mwachoonadi koma Iye; Ngwamphamvu zoposa, Ngwanzeru zakuya
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek