×

Ndipo iye amene atsutsana nawe pankhani za Yesu utalandira nzeru izi muuze 3:61 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:61) ayat 61 in Chichewa

3:61 Surah al-‘Imran ayat 61 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 61 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿فَمَنۡ حَآجَّكَ فِيهِ مِنۢ بَعۡدِ مَا جَآءَكَ مِنَ ٱلۡعِلۡمِ فَقُلۡ تَعَالَوۡاْ نَدۡعُ أَبۡنَآءَنَا وَأَبۡنَآءَكُمۡ وَنِسَآءَنَا وَنِسَآءَكُمۡ وَأَنفُسَنَا وَأَنفُسَكُمۡ ثُمَّ نَبۡتَهِلۡ فَنَجۡعَل لَّعۡنَتَ ٱللَّهِ عَلَى ٱلۡكَٰذِبِينَ ﴾
[آل عِمران: 61]

Ndipo iye amene atsutsana nawe pankhani za Yesu utalandira nzeru izi muuze kuti: “Bwerani kuti taitane ana athu ndi ana anu, akazi athu ndi akazi anu, ife ndi inu ndipo tipemphe modzichepetsa kuti matemberero a Mulungu akhale pa anthu amene ali nkunama.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فمن حاجك فيه من بعد ما جاءك من العلم فقل تعالوا ندع, باللغة نيانجا

﴿فمن حاجك فيه من بعد ما جاءك من العلم فقل تعالوا ندع﴾ [آل عِمران: 61]

Khaled Ibrahim Betala
“Tsopano amene akutsutsana nawe (iwe Mtumiki s.a.w) pa ichi pambuyo pokudzera kuzindikira, auze: “Bwerani tiitane ana athu ndi ana anu, akazi athu ndi akazi anu, ife ndi inu; kenako modzichepetsa tipemphe tembelero la Allah kuti likhale pa amene ali abodza (mwa ife).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek