×

Nena: “oh inu anthu a m’Buku! Bwerani ku Mau amene ndi oona 3:64 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:64) ayat 64 in Chichewa

3:64 Surah al-‘Imran ayat 64 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 64 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿قُلۡ يَٰٓأَهۡلَ ٱلۡكِتَٰبِ تَعَالَوۡاْ إِلَىٰ كَلِمَةٖ سَوَآءِۭ بَيۡنَنَا وَبَيۡنَكُمۡ أَلَّا نَعۡبُدَ إِلَّا ٱللَّهَ وَلَا نُشۡرِكَ بِهِۦ شَيۡـٔٗا وَلَا يَتَّخِذَ بَعۡضُنَا بَعۡضًا أَرۡبَابٗا مِّن دُونِ ٱللَّهِۚ فَإِن تَوَلَّوۡاْ فَقُولُواْ ٱشۡهَدُواْ بِأَنَّا مُسۡلِمُونَ ﴾
[آل عِمران: 64]

Nena: “oh inu anthu a m’Buku! Bwerani ku Mau amene ndi oona pakati pa inu ndi ife, kuti tisapembedze wina aliyense koma Mulungu mmodzi ndipo tisamuphatikize ndi china chili chonse ndipo pasakhale wina pakati pathu amene adzasankha ena ngati ambuye powonjezera pa Mulungu. Ndipo ngati iwo akana, nena: “Inu chitirani umboni kuti Ife ndife Asilamu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل ياأهل الكتاب تعالوا إلى كلمة سواء بيننا وبينكم ألا نعبد إلا, باللغة نيانجا

﴿قل ياأهل الكتاب تعالوا إلى كلمة سواء بيننا وبينكم ألا نعبد إلا﴾ [آل عِمران: 64]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “Inu eni buku (la Allah, Ayuda ndi Akhrisitu!) Idzani ku liwu lolingana pakati pathu ndi inu (lakuti) tisapembedze aliyense koma Allah (Mmodzi Yekha), ndiponso tisamphatikize ndi chilichonse ndipo ena mwa ife asawasandutse anzawo kukhala milungu m’malo mwa Allah.” Ngati atembenuka ndi kunyoza, nenani: “Ikirani umboni kuti ife ndife Asilamu (ogonjera malamulo a Allah).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek