×

“oh inu anthu a m’Buku! Kodi ndi chifukwa chiyani mukutsutsana za Abrahamu, 3:65 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:65) ayat 65 in Chichewa

3:65 Surah al-‘Imran ayat 65 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 65 - آل عِمران - Page - Juz 3

﴿يَٰٓأَهۡلَ ٱلۡكِتَٰبِ لِمَ تُحَآجُّونَ فِيٓ إِبۡرَٰهِيمَ وَمَآ أُنزِلَتِ ٱلتَّوۡرَىٰةُ وَٱلۡإِنجِيلُ إِلَّا مِنۢ بَعۡدِهِۦٓۚ أَفَلَا تَعۡقِلُونَ ﴾
[آل عِمران: 65]

“oh inu anthu a m’Buku! Kodi ndi chifukwa chiyani mukutsutsana za Abrahamu, pamene Buku la Chipangano chakale ndi Chipangano Chatsopano linali lisanavumbulutsidwe panthawi yake? Kodimulibenzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأهل الكتاب لم تحاجون في إبراهيم وما أنـزلت التوراة والإنجيل إلا من, باللغة نيانجا

﴿ياأهل الكتاب لم تحاجون في إبراهيم وما أنـزلت التوراة والإنجيل إلا من﴾ [آل عِمران: 65]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwapatsidwa buku! Bwanji mukutsutsana za Ibrahim pomwe Taurat ndi Injili sizidavumbulutsidwe koma pambuyo pake. Kodi simuzindikira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek