×

Ndithudi Nyumba yoyamba kuti anthu azipembedzeramo ndi ija imene idali ku Mecca, 3:96 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah al-‘Imran ⮕ (3:96) ayat 96 in Chichewa

3:96 Surah al-‘Imran ayat 96 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah al-‘Imran ayat 96 - آل عِمران - Page - Juz 4

﴿إِنَّ أَوَّلَ بَيۡتٖ وُضِعَ لِلنَّاسِ لَلَّذِي بِبَكَّةَ مُبَارَكٗا وَهُدٗى لِّلۡعَٰلَمِينَ ﴾
[آل عِمران: 96]

Ndithudi Nyumba yoyamba kuti anthu azipembedzeramo ndi ija imene idali ku Mecca, yodzadza ndi madalitso, ndi malangizo kwa anthu a mitundu yonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن أول بيت وضع للناس للذي ببكة مباركا وهدى للعالمين, باللغة نيانجا

﴿إن أول بيت وضع للناس للذي ببكة مباركا وهدى للعالمين﴾ [آل عِمران: 96]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi, nyumba yoyamba yomwe idakhazikitsidwa chifukwa cha anthu (kuti azipempheramo) ndiyomwe ili pa Bakka (ku Makka); yodalitsidwa ndiponso ndichiongolo kwa anthu onse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek