×

Pamene iwo adadza kwa inu kuchokera kumwamba ndi kuchokera padziko lapansi ndiponso 33:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:10) ayat 10 in Chichewa

33:10 Surah Al-Ahzab ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 10 - الأحزَاب - Page - Juz 21

﴿إِذۡ جَآءُوكُم مِّن فَوۡقِكُمۡ وَمِنۡ أَسۡفَلَ مِنكُمۡ وَإِذۡ زَاغَتِ ٱلۡأَبۡصَٰرُ وَبَلَغَتِ ٱلۡقُلُوبُ ٱلۡحَنَاجِرَ وَتَظُنُّونَ بِٱللَّهِ ٱلظُّنُونَا۠ ﴾
[الأحزَاب: 10]

Pamene iwo adadza kwa inu kuchokera kumwamba ndi kuchokera padziko lapansi ndiponso pamene maso adatembenuka, mitima yanu idafumuka mpaka pakhosi ndipo inu mudayamba kuganiza maganizo oipa okhudza Mulungu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ جاءوكم من فوقكم ومن أسفل منكم وإذ زاغت الأبصار وبلغت القلوب, باللغة نيانجا

﴿إذ جاءوكم من فوقكم ومن أسفل منكم وإذ زاغت الأبصار وبلغت القلوب﴾ [الأحزَاب: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Pamene adakudzerani cha kumtunda kwanu, ndi kunsi kwanu (kumtunda kwa dambo ndi kumunsi kwake), pamene maso adangoti tong’oo chammbali ndipo mitima idafika kum’mero (chifukwa cha mantha ndi kunjenjemera) uku mukumganizira Allah maganizo osiyanasiyana
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek