×

oh inu anthu okhulupirira! Kumbukirani chisomo cha Mulungu pa inu pamene kudadza 33:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:9) ayat 9 in Chichewa

33:9 Surah Al-Ahzab ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 9 - الأحزَاب - Page - Juz 21

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ ٱذۡكُرُواْ نِعۡمَةَ ٱللَّهِ عَلَيۡكُمۡ إِذۡ جَآءَتۡكُمۡ جُنُودٞ فَأَرۡسَلۡنَا عَلَيۡهِمۡ رِيحٗا وَجُنُودٗا لَّمۡ تَرَوۡهَاۚ وَكَانَ ٱللَّهُ بِمَا تَعۡمَلُونَ بَصِيرًا ﴾
[الأحزَاب: 9]

oh inu anthu okhulupirira! Kumbukirani chisomo cha Mulungu pa inu pamene kudadza gulu la adani. Koma Ife tidatumiza, kuti iwagonjetse, mphepo ya mkuntho ndi Asirikali amene inu simudawaone. Koma Mulungu amaona zonse zimene mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا اذكروا نعمة الله عليكم إذ جاءتكم جنود فأرسلنا عليهم, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا اذكروا نعمة الله عليكم إذ جاءتكم جنود فأرسلنا عليهم﴾ [الأحزَاب: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Kumbukirani chisomo cha Allah chimene chili pa inu, pamene adakudzerani magulu a nkhondo. Ndipo tidawatumizira mphepo ndi magulu a nkhondo (a angelo) amene simudawaone. Ndipo Allah akuona (zonse) zimene mukuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek