×

Ndipo mdani akadalowa kudzera pachipata cha mbali ina ya mzindawu, ndipo iwo 33:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:14) ayat 14 in Chichewa

33:14 Surah Al-Ahzab ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 14 - الأحزَاب - Page - Juz 21

﴿وَلَوۡ دُخِلَتۡ عَلَيۡهِم مِّنۡ أَقۡطَارِهَا ثُمَّ سُئِلُواْ ٱلۡفِتۡنَةَ لَأٓتَوۡهَا وَمَا تَلَبَّثُواْ بِهَآ إِلَّا يَسِيرٗا ﴾
[الأحزَاب: 14]

Ndipo mdani akadalowa kudzera pachipata cha mbali ina ya mzindawu, ndipo iwo akadafunsidwa kuti aleke chisilamu. Ndithudi, iwo akadachita chomwecho. Ndipo sakadakayika kutero, ngakhale mpang’ono pomwe

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو دخلت عليهم من أقطارها ثم سئلوا الفتنة لآتوها وما تلبثوا بها, باللغة نيانجا

﴿ولو دخلت عليهم من أقطارها ثم سئلوا الفتنة لآتوها وما تلبثوا بها﴾ [الأحزَاب: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo akadawalowera (magulu ankhondo a adaniwo), mbali zonse (za Mzindawo), kenako nkupemphedwa kuti atuluke m’Chisilamu ndi kumenyana ndi Asilamu, akadachita zimenezo; ndipo sakadayembekezera koma nthawi yochepa basi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek