×

Pakati pa okhulupirira pali anthu amene amakwaniritsa lonjezo limene adachita ndi Mulungu. 33:23 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:23) ayat 23 in Chichewa

33:23 Surah Al-Ahzab ayat 23 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 23 - الأحزَاب - Page - Juz 21

﴿مِّنَ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ رِجَالٞ صَدَقُواْ مَا عَٰهَدُواْ ٱللَّهَ عَلَيۡهِۖ فَمِنۡهُم مَّن قَضَىٰ نَحۡبَهُۥ وَمِنۡهُم مَّن يَنتَظِرُۖ وَمَا بَدَّلُواْ تَبۡدِيلٗا ﴾
[الأحزَاب: 23]

Pakati pa okhulupirira pali anthu amene amakwaniritsa lonjezo limene adachita ndi Mulungu. Ena mwa iwo adafa ndipo ena akadadikira. Koma iwo sadasinthe maganizo ngakhale pang’ono

❮ Previous Next ❯

ترجمة: من المؤمنين رجال صدقوا ما عاهدوا الله عليه فمنهم من قضى نحبه, باللغة نيانجا

﴿من المؤمنين رجال صدقوا ما عاهدوا الله عليه فمنهم من قضى نحبه﴾ [الأحزَاب: 23]

Khaled Ibrahim Betala
“Mwa okhulupirira alipo amuna ena amene adakwaniritsa zomwe adamlonjeza Allah (kuti sadzathawa pa nkhondo pamodzi ndi Mtumiki (s.a.w), ena mwa iwo adamaliza moyo wawo (nakwaniritsa lonjezo lawo pofera pa njira ya Allah). Ndipo ena mwa iwo akuyembekezerabe (kufera pa njira ya Allah). Ndipo sadasinthe konse (lonjezo lawo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek