×

Ndipo Mulungu adawabweza anthu osakhulupirira atakwiya. Iwo sadapeze chabwino china chilichonse ndipo 33:25 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:25) ayat 25 in Chichewa

33:25 Surah Al-Ahzab ayat 25 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 25 - الأحزَاب - Page - Juz 21

﴿وَرَدَّ ٱللَّهُ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ بِغَيۡظِهِمۡ لَمۡ يَنَالُواْ خَيۡرٗاۚ وَكَفَى ٱللَّهُ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ ٱلۡقِتَالَۚ وَكَانَ ٱللَّهُ قَوِيًّا عَزِيزٗا ﴾
[الأحزَاب: 25]

Ndipo Mulungu adawabweza anthu osakhulupirira atakwiya. Iwo sadapeze chabwino china chilichonse ndipo Mulungu adawathandiza anthu okhulupirira pomenya nkhondo. Ndipo Mulungu ndi wamphamvu zambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ورد الله الذين كفروا بغيظهم لم ينالوا خيرا وكفى الله المؤمنين القتال, باللغة نيانجا

﴿ورد الله الذين كفروا بغيظهم لم ينالوا خيرا وكفى الله المؤمنين القتال﴾ [الأحزَاب: 25]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Allah adawabweza amene sadakhulupirire uku ali odzazidwa ndi mkwiyo m’mitima mwawo; sadapeze chabwino; (sadagonjetse Asilamu ndi kupeza zimene ankaziyembekezera monga zotola za pa nkhondo). Ndipo Allah adawakwaniritsira okhulupirira nkhondo (powatumizira adani mphepo yamkuntho ndi angelo). Ndipo, Allah Ngwamphamvu, Ngopambana, (sapambanidwa ndi chilichonse)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek