×

Oh iwe Mtumwi! Auze akazi ako kuti, “Ngati inu mukonda moyo wa 33:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:28) ayat 28 in Chichewa

33:28 Surah Al-Ahzab ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 28 - الأحزَاب - Page - Juz 21

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلنَّبِيُّ قُل لِّأَزۡوَٰجِكَ إِن كُنتُنَّ تُرِدۡنَ ٱلۡحَيَوٰةَ ٱلدُّنۡيَا وَزِينَتَهَا فَتَعَالَيۡنَ أُمَتِّعۡكُنَّ وَأُسَرِّحۡكُنَّ سَرَاحٗا جَمِيلٗا ﴾
[الأحزَاب: 28]

Oh iwe Mtumwi! Auze akazi ako kuti, “Ngati inu mukonda moyo wa dziko lino ndiponso zosangalatsa zake, bwerani, ine ndidzakupatsani zosangalatsa zake ndipo ndidzakulolani kuti muchoke bwinobwino.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها النبي قل لأزواجك إن كنتن تردن الحياة الدنيا وزينتها فتعالين أمتعكن, باللغة نيانجا

﴿ياأيها النبي قل لأزواجك إن كنتن تردن الحياة الدنيا وزينتها فتعالين أمتعكن﴾ [الأحزَاب: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“E iwe Mneneri! Nena kwa akazi ako (m’njira yowalangiza): “Ngati mufuna moyo wa dziko lapansi ndi zosangalatsa zake (ine ndilibe zosangalatsa za m’dziko, ndipo sindingakukakamizeni kuti mukhale ndi ine mu moyo wa umphawi; ngati mufuna) bwerani ndikupatsani cholekanira, chokusangalatsani, kenako ndikusiyeni kusiyana kwabwino (kopanda masautso).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek