×

Ndipo usamvere zilakolako za anthu osakhulupirira ndi za anthu a chinyengo. Usalabadire 33:48 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:48) ayat 48 in Chichewa

33:48 Surah Al-Ahzab ayat 48 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 48 - الأحزَاب - Page - Juz 22

﴿وَلَا تُطِعِ ٱلۡكَٰفِرِينَ وَٱلۡمُنَٰفِقِينَ وَدَعۡ أَذَىٰهُمۡ وَتَوَكَّلۡ عَلَى ٱللَّهِۚ وَكَفَىٰ بِٱللَّهِ وَكِيلٗا ﴾
[الأحزَاب: 48]

Ndipo usamvere zilakolako za anthu osakhulupirira ndi za anthu a chinyengo. Usalabadire zonena zawo koma ika chikhulupiriro chako mwa Mulungu. Mulungu ndi wokwana kukhala Mtetezi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولا تطع الكافرين والمنافقين ودع أذاهم وتوكل على الله وكفى بالله وكيلا, باللغة نيانجا

﴿ولا تطع الكافرين والمنافقين ودع أذاهم وتوكل على الله وكفى بالله وكيلا﴾ [الأحزَاب: 48]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo usawamvere osakhulupirira ndi achiphamaso (pa zimene akufuna kuti uwapeputsire malamulo a Allah), usalabadire masautso awo, ndipo tsamira kwa Allah. Ndipo Allah akukwanira kukhala Mtetezi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek