×

Ndithudi iwo amene amanena zinthu zoipa zokhudza Mulungu ndi Mtumwi wake, Mulungu 33:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:57) ayat 57 in Chichewa

33:57 Surah Al-Ahzab ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 57 - الأحزَاب - Page - Juz 22

﴿إِنَّ ٱلَّذِينَ يُؤۡذُونَ ٱللَّهَ وَرَسُولَهُۥ لَعَنَهُمُ ٱللَّهُ فِي ٱلدُّنۡيَا وَٱلۡأٓخِرَةِ وَأَعَدَّ لَهُمۡ عَذَابٗا مُّهِينٗا ﴾
[الأحزَاب: 57]

Ndithudi iwo amene amanena zinthu zoipa zokhudza Mulungu ndi Mtumwi wake, Mulungu anawatemberera iwo m’moyo uno ndiponso adzawatemberera m’moyo umene uli nkudza ndipo wawakonzera chilango chochititsa manyazi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الذين يؤذون الله ورسوله لعنهم الله في الدنيا والآخرة وأعد لهم, باللغة نيانجا

﴿إن الذين يؤذون الله ورسوله لعنهم الله في الدنيا والآخرة وأعد لهم﴾ [الأحزَاب: 57]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu amene akumukwiyitsa Allah ndi kumuvutitsa Mtumiki Wake (ponyozera malamulo ake) Allah wawatembelera pa dziko lapansi (mpaka) pa tsiku la chimaliziro, ndipo wawakonzera chilango chosambula
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek