×

Oh iwe Mtumwi! Auze akazi ako ndi ana ako, akazi ndi akazi 33:59 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahzab ⮕ (33:59) ayat 59 in Chichewa

33:59 Surah Al-Ahzab ayat 59 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahzab ayat 59 - الأحزَاب - Page - Juz 22

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلنَّبِيُّ قُل لِّأَزۡوَٰجِكَ وَبَنَاتِكَ وَنِسَآءِ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ يُدۡنِينَ عَلَيۡهِنَّ مِن جَلَٰبِيبِهِنَّۚ ذَٰلِكَ أَدۡنَىٰٓ أَن يُعۡرَفۡنَ فَلَا يُؤۡذَيۡنَۗ وَكَانَ ٱللَّهُ غَفُورٗا رَّحِيمٗا ﴾
[الأحزَاب: 59]

Oh iwe Mtumwi! Auze akazi ako ndi ana ako, akazi ndi akazi a anthu okhulupirira kuti azivala moyenera zovala zawo zapamwamba zoonjezera pa zovala zomwe avala mkati. Zimenezi zidzakhala zabwino kuti akhoza kudziwika nazo ndipo kotero iwo sadzavutitsidwa ayi. Ndipo Mulungu ndi wokhululukira ndi Mwini chisoni chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها النبي قل لأزواجك وبناتك ونساء المؤمنين يدنين عليهن من جلابيبهن ذلك, باللغة نيانجا

﴿ياأيها النبي قل لأزواجك وبناتك ونساء المؤمنين يدنين عليهن من جلابيبهن ذلك﴾ [الأحزَاب: 59]

Khaled Ibrahim Betala
“E iwe Mneneri! Uza akazi ako, ndi ana ako aakazi, ndi akazi a okhulupirira, kuti adziphimbe ndi nsalu zawo (akamatuluka m’nyumba), kutero kuchititsa kuti adziwike, asazunzidwe (ndi anthu achipongwe). Ndipo Allah Ngokhululuka kwambiri Ngwachisoni
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek