×

Nena, “Kodi ndani amene amakupatsani zabwino kuchokera kumwamba ndi pa dziko lapansi?” 34:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:24) ayat 24 in Chichewa

34:24 Surah Saba’ ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 24 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿۞ قُلۡ مَن يَرۡزُقُكُم مِّنَ ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَٱلۡأَرۡضِۖ قُلِ ٱللَّهُۖ وَإِنَّآ أَوۡ إِيَّاكُمۡ لَعَلَىٰ هُدًى أَوۡ فِي ضَلَٰلٖ مُّبِينٖ ﴾
[سَبإ: 24]

Nena, “Kodi ndani amene amakupatsani zabwino kuchokera kumwamba ndi pa dziko lapansi?” Nena: “Mulungu.” Ndithudi mwina ife kapena inu muli pa njira yachilungamo kapena ochimwa zedi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل من يرزقكم من السموات والأرض قل الله وإنا أو إياكم لعلى, باللغة نيانجا

﴿قل من يرزقكم من السموات والأرض قل الله وإنا أو إياكم لعلى﴾ [سَبإ: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena (kwa iwo, iwe Mneneri {s.a.w}): “Kodi ndani amakupatsani rizq (zaulere) kuchokera kumwamba ndi pansi?” (Ngati sakuyankha chifukwa chodzitukumula), nena (kwa iwo): “Ndi Allah (Mmodzi, amene akukupatsani zopatsa zaulere zochokera kumwamba ndi pansi); ndipo ife kapena inu, tili pachiongoko kapena mkusokera koonekera.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek