×

Nena, “Ndilangizeni zimene inu muli kuzipembedza kuonjezera pa Mulungu. Iyayi! Iye ndi 34:27 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:27) ayat 27 in Chichewa

34:27 Surah Saba’ ayat 27 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 27 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿قُلۡ أَرُونِيَ ٱلَّذِينَ أَلۡحَقۡتُم بِهِۦ شُرَكَآءَۖ كـَلَّاۚ بَلۡ هُوَ ٱللَّهُ ٱلۡعَزِيزُ ٱلۡحَكِيمُ ﴾
[سَبإ: 27]

Nena, “Ndilangizeni zimene inu muli kuzipembedza kuonjezera pa Mulungu. Iyayi! Iye ndi Mulungu, Mwini mphamvu ndi Mwini nzeru.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل أروني الذين ألحقتم به شركاء كلا بل هو الله العزيز الحكيم, باللغة نيانجا

﴿قل أروني الذين ألحقتم به شركاء كلا بل هو الله العزيز الحكيم﴾ [سَبإ: 27]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena (kwa iwo): “Ndisonyezeni amene mwawalumikiza ndi Iye monga othandizana Naye; iyayi, sizingatheke (Iye kukhala ndi anzake), koma Iye (Yekha) ndiye Allah, Mwini Mphamvu zoposa, Wanzeru zakuya.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek