×

Pamene chiphunzitso chathu chomveka chimalalikiridwa kwa iwo, iwo amati, “Uyu ndi munthu 34:43 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Saba’ ⮕ (34:43) ayat 43 in Chichewa

34:43 Surah Saba’ ayat 43 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Saba’ ayat 43 - سَبإ - Page - Juz 22

﴿وَإِذَا تُتۡلَىٰ عَلَيۡهِمۡ ءَايَٰتُنَا بَيِّنَٰتٖ قَالُواْ مَا هَٰذَآ إِلَّا رَجُلٞ يُرِيدُ أَن يَصُدَّكُمۡ عَمَّا كَانَ يَعۡبُدُ ءَابَآؤُكُمۡ وَقَالُواْ مَا هَٰذَآ إِلَّآ إِفۡكٞ مُّفۡتَرٗىۚ وَقَالَ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ لِلۡحَقِّ لَمَّا جَآءَهُمۡ إِنۡ هَٰذَآ إِلَّا سِحۡرٞ مُّبِينٞ ﴾
[سَبإ: 43]

Pamene chiphunzitso chathu chomveka chimalalikiridwa kwa iwo, iwo amati, “Uyu ndi munthu amene afuna kukuletsani chipembedzo cha makolo anu.” Ndipo iwo amati, “Ili ndi bodza limene wapeka.” Ndipo anthu osakhulupirira, pamene choonadi chidza kwa iwo amati, “Awa ndi matsenga.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذا تتلى عليهم آياتنا بينات قالوا ما هذا إلا رجل يريد أن, باللغة نيانجا

﴿وإذا تتلى عليهم آياتنا بينات قالوا ما هذا إلا رجل يريد أن﴾ [سَبإ: 43]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Ayah Zathu zofotokoza momveka zikamawerengedwa kwa iwo, amanena, “Sichina uyu (Muhammad {s.a.w}) koma ndi munthu yemwe akufuna kukutsekerezani mapemphero amene amapemphera makolo anu.” Ndipo akunena: “Sichina iyi (Qur’an) koma ndibodza lopekedwa.” Ndipo amene sadakhulupirire akunena pa choona pamene chawadzera: “Sikanthu ichi, koma ndi matsenga woonekera.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek