×

Ndipo zamoyo ndi zakufa sizifanana. Ndithudi Mulungu akhoza kumupanga aliyense amene wamufuna 35:22 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah FaTir ⮕ (35:22) ayat 22 in Chichewa

35:22 Surah FaTir ayat 22 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah FaTir ayat 22 - فَاطِر - Page - Juz 22

﴿وَمَا يَسۡتَوِي ٱلۡأَحۡيَآءُ وَلَا ٱلۡأَمۡوَٰتُۚ إِنَّ ٱللَّهَ يُسۡمِعُ مَن يَشَآءُۖ وَمَآ أَنتَ بِمُسۡمِعٖ مَّن فِي ٱلۡقُبُورِ ﴾
[فَاطِر: 22]

Ndipo zamoyo ndi zakufa sizifanana. Ndithudi Mulungu akhoza kumupanga aliyense amene wamufuna kuti amve koma iwe siungathe kuwauza iwo amene ali m’manda kuti amve

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما يستوي الأحياء ولا الأموات إن الله يسمع من يشاء وما أنت, باللغة نيانجا

﴿وما يستوي الأحياء ولا الأموات إن الله يسمع من يشاء وما أنت﴾ [فَاطِر: 22]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amoyo ndi akufa safanana (amene mitima yawo ili ndi moyo pokhala ndi chikhulupiliro, ndi amene mitima yawo ili yakufa posakhala ndi chikhulupiliro, ngosafanana). Ndithu Allah akumumveretsa amene wam’funa; koma iwe sungathe kumumveretsa amene ali m’manda
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek