×

Pali kusiyana m’maonekedwe pakati pa anthu, zolengedwa ndi zinyama. Iwo amene amaopa 35:28 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah FaTir ⮕ (35:28) ayat 28 in Chichewa

35:28 Surah FaTir ayat 28 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah FaTir ayat 28 - فَاطِر - Page - Juz 22

﴿وَمِنَ ٱلنَّاسِ وَٱلدَّوَآبِّ وَٱلۡأَنۡعَٰمِ مُخۡتَلِفٌ أَلۡوَٰنُهُۥ كَذَٰلِكَۗ إِنَّمَا يَخۡشَى ٱللَّهَ مِنۡ عِبَادِهِ ٱلۡعُلَمَٰٓؤُاْۗ إِنَّ ٱللَّهَ عَزِيزٌ غَفُورٌ ﴾
[فَاطِر: 28]

Pali kusiyana m’maonekedwe pakati pa anthu, zolengedwa ndi zinyama. Iwo amene amaopa Mulungu pakati pa akapolo ake ndiwo amene ali ndi nzeru chifukwa Mulungu ndi wamphamvu zambiri ndi wokhululukira nthawi zonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ومن الناس والدواب والأنعام مختلف ألوانه كذلك إنما يخشى الله من عباده, باللغة نيانجا

﴿ومن الناس والدواب والأنعام مختلف ألوانه كذلك إنما يخشى الله من عباده﴾ [فَاطِر: 28]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo mwa anthu ndi nyama zokwawa, ndi ziweto, nchimodzimodzinso; nzosiyana maonekedwe ake (utoto wake). Ndithu odziwa ndi amene amamuopa Allah mwa akapolo Ake. Ndithu Allah Ngwamphamvu zoposa; Ngokhululuka kwambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek