×

Ndipo iwo adzalira pofuna chipulumutso nati, “Ambuye wathu! Tichotseni kuno. Ife tikachita 35:37 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah FaTir ⮕ (35:37) ayat 37 in Chichewa

35:37 Surah FaTir ayat 37 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah FaTir ayat 37 - فَاطِر - Page - Juz 22

﴿وَهُمۡ يَصۡطَرِخُونَ فِيهَا رَبَّنَآ أَخۡرِجۡنَا نَعۡمَلۡ صَٰلِحًا غَيۡرَ ٱلَّذِي كُنَّا نَعۡمَلُۚ أَوَلَمۡ نُعَمِّرۡكُم مَّا يَتَذَكَّرُ فِيهِ مَن تَذَكَّرَ وَجَآءَكُمُ ٱلنَّذِيرُۖ فَذُوقُواْ فَمَا لِلظَّٰلِمِينَ مِن نَّصِيرٍ ﴾
[فَاطِر: 37]

Ndipo iwo adzalira pofuna chipulumutso nati, “Ambuye wathu! Tichotseni kuno. Ife tikachita zinthu zabwino kusiyana ndi zimene tinali kuchita”. “Kodi Ife sitidakusungeni ndi moyo nthawi yaitali kuti iye amene amalabadira akadazindikira za zimenezi? Ndipo kwa inu kudadza mchenjezi kotero lawani chilango chifukwa munthu wochimwa alibe woti angamuthandize”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وهم يصطرخون فيها ربنا أخرجنا نعمل صالحا غير الذي كنا نعمل أو, باللغة نيانجا

﴿وهم يصطرخون فيها ربنا أخرجنا نعمل صالحا غير الذي كنا نعمل أو﴾ [فَاطِر: 37]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo m’menemo iwo adzakuwa (adzalira uku akunena): “Mbuye wathu! Titulutseni (m’Moto ndi kutibweza pa dziko lapansi); tikachita ntchito zabwino, osati zija tinkachita.” (Allah adzawauza): “Kodi sitidakupatseni moyo wokwanira wotheka kukumbuka kwa wokumbuka? Ndiponso mchenjezi adakudzerani. Choncho lawani (chilango). Ndipo anthu ochita zoipa alibe mpulumutsi.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek