×

Kodi iye,amene zoipa zake zimaoneka ngati zabwino, moti akamaziona amati ndi zabwino? 35:8 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah FaTir ⮕ (35:8) ayat 8 in Chichewa

35:8 Surah FaTir ayat 8 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah FaTir ayat 8 - فَاطِر - Page - Juz 22

﴿أَفَمَن زُيِّنَ لَهُۥ سُوٓءُ عَمَلِهِۦ فَرَءَاهُ حَسَنٗاۖ فَإِنَّ ٱللَّهَ يُضِلُّ مَن يَشَآءُ وَيَهۡدِي مَن يَشَآءُۖ فَلَا تَذۡهَبۡ نَفۡسُكَ عَلَيۡهِمۡ حَسَرَٰتٍۚ إِنَّ ٱللَّهَ عَلِيمُۢ بِمَا يَصۡنَعُونَ ﴾
[فَاطِر: 8]

Kodi iye,amene zoipa zake zimaoneka ngati zabwino, moti akamaziona amati ndi zabwino? Ndithudi Mulungu amasocheretsa aliyense amene amamufuna ndiponso amatsogolera aliyense amene wamufuna. Kotero usavutike mu mtima mwako chifukwa cha iwo. Ndithudi Mulungu amadziwa zonse zimene amachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفمن زين له سوء عمله فرآه حسنا فإن الله يضل من يشاء, باللغة نيانجا

﴿أفمن زين له سوء عمله فرآه حسنا فإن الله يضل من يشاء﴾ [فَاطِر: 8]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi amene zochita zake zoipa zakometsedwa kwa iye nkumaziona kuti nzabwino, (ngolingana ndi amene waongoka ndi chiongoko cha Allah kotero kuti chabwino nkuchiyesa chabwino; choipa nkuchiyesa choipa?) Ndithu Allah akumlekelera kuti asokere yemwe wamfuna (chifukwa chakuti safuna kuongoka), ndipo akuongola amene wam’funa. Choncho moyo wako usaonongeke chifukwa chowadandaula iwo. Ndithu Allah Ngodziwa zonse zimene (iwo) akuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek