×

Ife sitidamuphunzitse iye ndakatulo ayi ndiponso si koyenera kuti akhale mlakatuli. Ichi 36:69 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ya-Sin ⮕ (36:69) ayat 69 in Chichewa

36:69 Surah Ya-Sin ayat 69 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ya-Sin ayat 69 - يسٓ - Page - Juz 23

﴿وَمَا عَلَّمۡنَٰهُ ٱلشِّعۡرَ وَمَا يَنۢبَغِي لَهُۥٓۚ إِنۡ هُوَ إِلَّا ذِكۡرٞ وَقُرۡءَانٞ مُّبِينٞ ﴾
[يسٓ: 69]

Ife sitidamuphunzitse iye ndakatulo ayi ndiponso si koyenera kuti akhale mlakatuli. Ichi si china koma chikumbutso ndi dongosolo la Korani

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما علمناه الشعر وما ينبغي له إن هو إلا ذكر وقرآن مبين, باللغة نيانجا

﴿وما علمناه الشعر وما ينبغي له إن هو إلا ذكر وقرآن مبين﴾ [يسٓ: 69]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo sitidamphunzitse (Mtumiki {s.a.w}) ndakatulo, ndipo nkosayenera kwa iye (kukhala mlakatuli). Qur’an sichina, koma ndichikumbutso ndi buku lomwe likulongosola chilichonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek