×

Kodi iye amene adzapanga nkhope yake kukhala chishango cha chilango chowawa cha 39:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:24) ayat 24 in Chichewa

39:24 Surah Az-Zumar ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 24 - الزُّمَر - Page - Juz 23

﴿أَفَمَن يَتَّقِي بِوَجۡهِهِۦ سُوٓءَ ٱلۡعَذَابِ يَوۡمَ ٱلۡقِيَٰمَةِۚ وَقِيلَ لِلظَّٰلِمِينَ ذُوقُواْ مَا كُنتُمۡ تَكۡسِبُونَ ﴾
[الزُّمَر: 24]

Kodi iye amene adzapanga nkhope yake kukhala chishango cha chilango chowawa cha tsiku louka kwa akufa adzakhala wofanana ndi iye amene wapulumuka? Ndipo zidzanenedwa kwa anthu ochimwa kuti, “Lawani zipatso za ntchito zanu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفمن يتقي بوجهه سوء العذاب يوم القيامة وقيل للظالمين ذوقوا ما كنتم, باللغة نيانجا

﴿أفمن يتقي بوجهه سوء العذاب يوم القيامة وقيل للظالمين ذوقوا ما كنتم﴾ [الزُّمَر: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi yemwe adzakhala akudzitchinjiriza ndi nkhope yake (uku manja atanjatidwa) ku chilango choipa pa tsiku la Qiyâma, (angafanane ndi yemwe adzakhala mchisangalalo mminda ya mtendere?” Ndipo kudzanenedwa kwa oipa: “Lawani zoipa za zochita zanu.”)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek