×

Ndithudi tavumbulutsa kwa iwe Buku la ulangizi kwa anthu mwachoonadi. Kotero aliyense 39:41 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:41) ayat 41 in Chichewa

39:41 Surah Az-Zumar ayat 41 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 41 - الزُّمَر - Page - Juz 24

﴿إِنَّآ أَنزَلۡنَا عَلَيۡكَ ٱلۡكِتَٰبَ لِلنَّاسِ بِٱلۡحَقِّۖ فَمَنِ ٱهۡتَدَىٰ فَلِنَفۡسِهِۦۖ وَمَن ضَلَّ فَإِنَّمَا يَضِلُّ عَلَيۡهَاۖ وَمَآ أَنتَ عَلَيۡهِم بِوَكِيلٍ ﴾
[الزُّمَر: 41]

Ndithudi tavumbulutsa kwa iwe Buku la ulangizi kwa anthu mwachoonadi. Kotero aliyense amene atsatira njira yoyenera amapulumutsa mzimu wake ndipo aliyense amene asochera alanga mzimu wake. Ndipo iwe sindiwe msungi wawo ayi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إنا أنـزلنا عليك الكتاب للناس بالحق فمن اهتدى فلنفسه ومن ضل فإنما, باللغة نيانجا

﴿إنا أنـزلنا عليك الكتاب للناس بالحق فمن اهتدى فلنفسه ومن ضل فإنما﴾ [الزُّمَر: 41]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu ife takuvumbulutsira buku ili chifukwa cha anthu (onse) kuti Tiwafotokozere choona. Choncho amene waongoka, zabwino zake nza iye mwini. Koma amene wakhota, ndiye kuti akudzikhotetsa yekha. (Ndipo zoipa za kukhotako zidzakhala pa iye yekha). Ndipo iwe si muyang’anili wawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek