×

Ndi Mulungu amene amachotsa mizimu ya anthu pa nthawi ya imfa ndi 39:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:42) ayat 42 in Chichewa

39:42 Surah Az-Zumar ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 42 - الزُّمَر - Page - Juz 24

﴿ٱللَّهُ يَتَوَفَّى ٱلۡأَنفُسَ حِينَ مَوۡتِهَا وَٱلَّتِي لَمۡ تَمُتۡ فِي مَنَامِهَاۖ فَيُمۡسِكُ ٱلَّتِي قَضَىٰ عَلَيۡهَا ٱلۡمَوۡتَ وَيُرۡسِلُ ٱلۡأُخۡرَىٰٓ إِلَىٰٓ أَجَلٖ مُّسَمًّىۚ إِنَّ فِي ذَٰلِكَ لَأٓيَٰتٖ لِّقَوۡمٖ يَتَفَكَّرُونَ ﴾
[الزُّمَر: 42]

Ndi Mulungu amene amachotsa mizimu ya anthu pa nthawi ya imfa ndi mizimu ya anthu a moyo akamagona. Iye amasunga mizimu ya amene adalamula kuti afe ndi kubweza mizimu ya ena mpaka nthawi yawo itakwana. Ndithudi mu zimenezi muli zizindikiro kwa iwo amene amaganiza kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الله يتوفى الأنفس حين موتها والتي لم تمت في منامها فيمسك التي, باللغة نيانجا

﴿الله يتوفى الأنفس حين موتها والتي لم تمت في منامها فيمسك التي﴾ [الزُّمَر: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah ndiye amatenga mizimu pa nthawi ya imfa yake ndipo amatenga mizimu yomwe siidafe panthawi yogona tulo. Ndipo amaigwira mizimu imene wailamula kufa, (osaibwezera ku matupi awo). Koma inayo amaitumiza (kumatupi awo, yomwe nthawi yake siidakwane) kuti ikwaniritse nthawi yake imene idaikidwa. Ndithu m’zimenezi muli zisonyezo kwa anthu olingalira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek