×

Koma pakadapanda Chisomo ndi Chisoni cha Mulungu pa iwe gulu lina la 4:113 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:113) ayat 113 in Chichewa

4:113 Surah An-Nisa’ ayat 113 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 113 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَلَوۡلَا فَضۡلُ ٱللَّهِ عَلَيۡكَ وَرَحۡمَتُهُۥ لَهَمَّت طَّآئِفَةٞ مِّنۡهُمۡ أَن يُضِلُّوكَ وَمَا يُضِلُّونَ إِلَّآ أَنفُسَهُمۡۖ وَمَا يَضُرُّونَكَ مِن شَيۡءٖۚ وَأَنزَلَ ٱللَّهُ عَلَيۡكَ ٱلۡكِتَٰبَ وَٱلۡحِكۡمَةَ وَعَلَّمَكَ مَا لَمۡ تَكُن تَعۡلَمُۚ وَكَانَ فَضۡلُ ٱللَّهِ عَلَيۡكَ عَظِيمٗا ﴾
[النِّسَاء: 113]

Koma pakadapanda Chisomo ndi Chisoni cha Mulungu pa iwe gulu lina la iwo likadafuna kuti likusokeretse koma iwo sangasokeretse wina aliyense koma iwo okha, ndipo iwo sangakupweteke iwe ayi. Mulungu wavumbulutsa kwa iwe Buku la luntha ndi kukuphunzitsa iwe zinthu zimene siunali kuzidziwa. Ndipo ubwino wa Mulungu pa iwe ndi waukulu zedi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولولا فضل الله عليك ورحمته لهمت طائفة منهم أن يضلوك وما يضلون, باللغة نيانجا

﴿ولولا فضل الله عليك ورحمته لهمت طائفة منهم أن يضلوك وما يضلون﴾ [النِّسَاء: 113]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pakadapanda ubwino wa Allah ndi chisoni chake pa iwe, ndithudi, gulu limodzi la iwo likadalinga kukusokeretsa. Ndipo iwo palibe yemwe akadamsokeretsa koma iwo okha basi. Ndipo sangathe kukuvutitsa ndi chilichonse. Ndipo Allah wakuvumbulutsira buku, kudzanso luntha. Ndipo wakuphunzitsa zomwe sudali kuzidziwa. Ndipo ubwino wa Allah umene uli pa iwe ngwaukulu zedi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek