×

Mulibe zabwino zambiri muzokambirana zawo za mseri kupatula mwa iye amene amalangiza 4:114 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:114) ayat 114 in Chichewa

4:114 Surah An-Nisa’ ayat 114 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 114 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿۞ لَّا خَيۡرَ فِي كَثِيرٖ مِّن نَّجۡوَىٰهُمۡ إِلَّا مَنۡ أَمَرَ بِصَدَقَةٍ أَوۡ مَعۡرُوفٍ أَوۡ إِصۡلَٰحِۭ بَيۡنَ ٱلنَّاسِۚ وَمَن يَفۡعَلۡ ذَٰلِكَ ٱبۡتِغَآءَ مَرۡضَاتِ ٱللَّهِ فَسَوۡفَ نُؤۡتِيهِ أَجۡرًا عَظِيمٗا ﴾
[النِّسَاء: 114]

Mulibe zabwino zambiri muzokambirana zawo za mseri kupatula mwa iye amene amalangiza za kupereka chaulere, kuonetsa chifundo ndi chiyanjanitso pakati pa anthu, ndipo iye amene amachita izi ndi cholinga chokondweretsa Mulungu, Ife tidzampatsa mphotho yaikulu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لا خير في كثير من نجواهم إلا من أمر بصدقة أو معروف, باللغة نيانجا

﴿لا خير في كثير من نجواهم إلا من أمر بصدقة أو معروف﴾ [النِّسَاء: 114]

Khaled Ibrahim Betala
“Palibe ubwino m’zambiri zimene akunong’onezana kupatula amene akulamulira ena kupereka sadaka, kapena kuchita zabwino, kapenanso kuyanjanitsa pakati pa anthu (pakunong’onezana mawu). Amene angachite zimenezi, chifukwa chofuna chiyanjo cha Allah, tidzampatsa malipiro aakulu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek