×

Ndithudi! Mulungu sadzakhululukira munthu wopembedza mafano. Iye adzakhululukira wina aliyense amene wamufuna 4:116 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:116) ayat 116 in Chichewa

4:116 Surah An-Nisa’ ayat 116 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 116 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿إِنَّ ٱللَّهَ لَا يَغۡفِرُ أَن يُشۡرَكَ بِهِۦ وَيَغۡفِرُ مَا دُونَ ذَٰلِكَ لِمَن يَشَآءُۚ وَمَن يُشۡرِكۡ بِٱللَّهِ فَقَدۡ ضَلَّ ضَلَٰلَۢا بَعِيدًا ﴾
[النِّسَاء: 116]

Ndithudi! Mulungu sadzakhululukira munthu wopembedza mafano. Iye adzakhululukira wina aliyense amene wamufuna pa machimo ena onse ndipo aliyense amene amalambira milungu ina osati Mulungu, iye wasochera kwambiri kuchokera ku choonadi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن الله لا يغفر أن يشرك به ويغفر ما دون ذلك لمن, باللغة نيانجا

﴿إن الله لا يغفر أن يشرك به ويغفر ما دون ذلك لمن﴾ [النِّسَاء: 116]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi, Allah sakhululuka (uchimo) womphatikiza ndi chinthu china, (pochiyesa kuti ndi mnzake wa Allah). Koma Iye amakhululukira machimo ena omwe sali amenewo kwa yemwe wamfuna. Ndipo yemwe angamphatikize Allah (ndi milungu yabodza), ndithudi, wasokera kusokera konka nako kutali (ndi njira yachoonadi)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek