×

Ndipo zavumbulutsidwa kale kwa inu m’Buku kuti pamene inu mukumva chivumbulutso cha 4:140 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:140) ayat 140 in Chichewa

4:140 Surah An-Nisa’ ayat 140 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 140 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَقَدۡ نَزَّلَ عَلَيۡكُمۡ فِي ٱلۡكِتَٰبِ أَنۡ إِذَا سَمِعۡتُمۡ ءَايَٰتِ ٱللَّهِ يُكۡفَرُ بِهَا وَيُسۡتَهۡزَأُ بِهَا فَلَا تَقۡعُدُواْ مَعَهُمۡ حَتَّىٰ يَخُوضُواْ فِي حَدِيثٍ غَيۡرِهِۦٓ إِنَّكُمۡ إِذٗا مِّثۡلُهُمۡۗ إِنَّ ٱللَّهَ جَامِعُ ٱلۡمُنَٰفِقِينَ وَٱلۡكَٰفِرِينَ فِي جَهَنَّمَ جَمِيعًا ﴾
[النِّسَاء: 140]

Ndipo zavumbulutsidwa kale kwa inu m’Buku kuti pamene inu mukumva chivumbulutso cha Mulungu chili kukanidwa kapena kunyozedwa, inu musakhale pa malo amenewo mpaka pamene ayamba kukamba nkhani zina chifukwa mukakhala nawo, mudzakhala ngati iwo. Ndithudi Mulungu adzasonkhanitsa anthu a chinyengo ndi anthu osakhulupirira ku Gahena

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقد نـزل عليكم في الكتاب أن إذا سمعتم آيات الله يكفر بها, باللغة نيانجا

﴿وقد نـزل عليكم في الكتاب أن إذا سمعتم آيات الله يكفر بها﴾ [النِّسَاء: 140]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi Iye wakuvumbulutsirani m’buku (ili) kuti mukamva ma Ayah (ndime) a Allah akukanidwa ndi kuchitiridwa chipongwe, musakhale pamodzi nawo mpaka alowe m’zokamba zina. (Ngati mutakhala nawo) ndiye kuti mukhala chimodzimodzi ndi iwo. Ndithudi, Allah adzawasonkhanitsa achiphamaso ndi osakhulupirira onse m’moto wa Jahannam
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek