×

Ndipo palibe mmodzi wa anthu a m’Buku amene angakhulupirire mwa iye, asadafe. 4:159 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:159) ayat 159 in Chichewa

4:159 Surah An-Nisa’ ayat 159 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 159 - النِّسَاء - Page - Juz 6

﴿وَإِن مِّنۡ أَهۡلِ ٱلۡكِتَٰبِ إِلَّا لَيُؤۡمِنَنَّ بِهِۦ قَبۡلَ مَوۡتِهِۦۖ وَيَوۡمَ ٱلۡقِيَٰمَةِ يَكُونُ عَلَيۡهِمۡ شَهِيدٗا ﴾
[النِّسَاء: 159]

Ndipo palibe mmodzi wa anthu a m’Buku amene angakhulupirire mwa iye, asadafe. Ndipo patsiku louka kwa akufa, iye adzakhala mboni yowatsutsa iwo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإن من أهل الكتاب إلا ليؤمنن به قبل موته ويوم القيامة يكون, باللغة نيانجا

﴿وإن من أهل الكتاب إلا ليؤمنن به قبل موته ويوم القيامة يكون﴾ [النِّسَاء: 159]

Khaled Ibrahim Betala
“Palibe aliyense mwa anthu omwe adapatsidwa buku (Ayuda ndi Akhrisitu) koma kuti azamkhulupirira iye (Yesu kuti sadali mulungu) imfa yake (Yesuyo) isadadze (izi zizachitika pamene Yesuyo azabwerenso padziko lapansi kumapeto kwa dziko). Nayenso (Yesu) pa siku la chiweruziro adzaikira umboni pa iwo (kuti iye adali chabe kapolo wa Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek