×

Kodi kapena iwo ali ndi gawo mu Ufumu? Zikadatero, iwo sakadawapatsa anthu 4:53 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:53) ayat 53 in Chichewa

4:53 Surah An-Nisa’ ayat 53 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 53 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿أَمۡ لَهُمۡ نَصِيبٞ مِّنَ ٱلۡمُلۡكِ فَإِذٗا لَّا يُؤۡتُونَ ٱلنَّاسَ نَقِيرًا ﴾
[النِّسَاء: 53]

Kodi kapena iwo ali ndi gawo mu Ufumu? Zikadatero, iwo sakadawapatsa anthu ngakhale kanthu kakang’ono

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أم لهم نصيب من الملك فإذا لا يؤتون الناس نقيرا, باللغة نيانجا

﴿أم لهم نصيب من الملك فإذا لا يؤتون الناس نقيرا﴾ [النِّسَاء: 53]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi ali ndi gawo la ufumu (wa Allah? Nchifukwa ninji akunyasidwa munthu wina akaninkhidwa utumiki)? Zikadatero ndiye kuti sakadawapatsa anthu ngakhale kochepa kwambiri monga khokho la tende
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek