×

oh inu anthu okhulupirira! Mverani Mulungu ndipo mverani Mtumwi wake ndiponso iwo 4:59 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:59) ayat 59 in Chichewa

4:59 Surah An-Nisa’ ayat 59 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 59 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ أَطِيعُواْ ٱللَّهَ وَأَطِيعُواْ ٱلرَّسُولَ وَأُوْلِي ٱلۡأَمۡرِ مِنكُمۡۖ فَإِن تَنَٰزَعۡتُمۡ فِي شَيۡءٖ فَرُدُّوهُ إِلَى ٱللَّهِ وَٱلرَّسُولِ إِن كُنتُمۡ تُؤۡمِنُونَ بِٱللَّهِ وَٱلۡيَوۡمِ ٱلۡأٓخِرِۚ ذَٰلِكَ خَيۡرٞ وَأَحۡسَنُ تَأۡوِيلًا ﴾
[النِّسَاء: 59]

oh inu anthu okhulupirira! Mverani Mulungu ndipo mverani Mtumwi wake ndiponso iwo amene ali ndi udindo pakati panu. Ndipo ngati mutsutsana pa chinthu china chilichonse, chiperekeni icho kwa Mulungu ndi Mtumwi wake ngati inu mumakhulupirira mwa Mulungu ndi tsiku lomaliza. Zimenezi zidzakhala zabwino ndi zolungama pomaliza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا أطيعوا الله وأطيعوا الرسول وأولي الأمر منكم فإن تنازعتم, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا أطيعوا الله وأطيعوا الرسول وأولي الأمر منكم فإن تنازعتم﴾ [النِّسَاء: 59]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Mumvereni Allah ndiponso mumvereni Mtumiki, ndi omwe ali ndi udindo pa inu. Ngati Mutatsutsana pa chinthu chilichonse, chibwezeni kwa Allah ndi Mtumiki Wake, ngatidi mukukhulupirira Allah ndi tsiku lachimaliziro, kutero ndibwino; ndipo zotere zili ndi zotsatira zabwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek