×

Aliyense amene amvera Mtumwi ndithudi amvera Mulungu ndipo iye amene safuna kukumvera 4:80 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:80) ayat 80 in Chichewa

4:80 Surah An-Nisa’ ayat 80 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 80 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿مَّن يُطِعِ ٱلرَّسُولَ فَقَدۡ أَطَاعَ ٱللَّهَۖ وَمَن تَوَلَّىٰ فَمَآ أَرۡسَلۡنَٰكَ عَلَيۡهِمۡ حَفِيظٗا ﴾
[النِّسَاء: 80]

Aliyense amene amvera Mtumwi ndithudi amvera Mulungu ndipo iye amene safuna kukumvera iwe, Ife sitidakutumize kuti ukhale wowayang’anira ayi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: من يطع الرسول فقد أطاع الله ومن تولى فما أرسلناك عليهم حفيظا, باللغة نيانجا

﴿من يطع الرسول فقد أطاع الله ومن تولى فما أرسلناك عليهم حفيظا﴾ [النِّسَاء: 80]

Khaled Ibrahim Betala
“Yemwe angamvere Mtumiki ndiye kuti wamvera Allah, (chifukwa chakuti zonse zomwe iye akulamula nzotumidwa ndi Allah). Ndipo amene atembenukire kutali (kunyoza iwe, ndiye kuti zoipa zili pa iye mwini). Sitidakutumize iweyo kukhala muyang’anili pa iwo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek