×

Alekeni iwo amene amafunira zabwino ana awo, pamene iwo akufa, kuti asamale 4:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:9) ayat 9 in Chichewa

4:9 Surah An-Nisa’ ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 9 - النِّسَاء - Page - Juz 4

﴿وَلۡيَخۡشَ ٱلَّذِينَ لَوۡ تَرَكُواْ مِنۡ خَلۡفِهِمۡ ذُرِّيَّةٗ ضِعَٰفًا خَافُواْ عَلَيۡهِمۡ فَلۡيَتَّقُواْ ٱللَّهَ وَلۡيَقُولُواْ قَوۡلٗا سَدِيدًا ﴾
[النِّسَاء: 9]

Alekeni iwo amene amafunira zabwino ana awo, pamene iwo akufa, kuti asamale posawalakwira ana amasiye. Alekeni kuti aope Mulungu ndi kunena zinthu zokhazikitsa choonadi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وليخش الذين لو تركوا من خلفهم ذرية ضعافا خافوا عليهم فليتقوا الله, باللغة نيانجا

﴿وليخش الذين لو تركوا من خلفهم ذرية ضعافا خافوا عليهم فليتقوا الله﴾ [النِّسَاء: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (wowasiirawo) aope (kusachita chilungamo), kuti naonso ngati atasiya ana awo ofooka pambuyo, akadawaopera (kuchenjeleredwa). Choncho aope Allah ndipo anene mawu olingana (kwa ana amasiyewo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek