×

Akakhala anthu a Thamoud Ife tidawalangiza njira yoyenera koma iwo adasankha kuchita 41:17 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Fussilat ⮕ (41:17) ayat 17 in Chichewa

41:17 Surah Fussilat ayat 17 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Fussilat ayat 17 - فُصِّلَت - Page - Juz 24

﴿وَأَمَّا ثَمُودُ فَهَدَيۡنَٰهُمۡ فَٱسۡتَحَبُّواْ ٱلۡعَمَىٰ عَلَى ٱلۡهُدَىٰ فَأَخَذَتۡهُمۡ صَٰعِقَةُ ٱلۡعَذَابِ ٱلۡهُونِ بِمَا كَانُواْ يَكۡسِبُونَ ﴾
[فُصِّلَت: 17]

Akakhala anthu a Thamoud Ife tidawalangiza njira yoyenera koma iwo adasankha kuchita zoipa m’malo mochita zabwino kotero kwa iwo kudadza chilango chochititsa manyazi chifukwa cha ntchito zawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأما ثمود فهديناهم فاستحبوا العمى على الهدى فأخذتهم صاعقة العذاب الهون بما, باللغة نيانجا

﴿وأما ثمود فهديناهم فاستحبوا العمى على الهدى فأخذتهم صاعقة العذاب الهون بما﴾ [فُصِّلَت: 17]

Khaled Ibrahim Betala
“Naonso Asamudu tidawasonyeza (njira yabwino ndi njira yoipa), ndipo adakonda ndi kusankha kusokera kusiya chiongoko; ndipo udawapeza nkuwe wa chilango choyalutsa chifukwa cha machimo amene adali kuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek