×

Iye wakukhazikitsirani chipembedzo chimene adakhazikitsira Nowa kuti atsatire, ndi chimene tavumbulutsa kwa 42:13 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:13) ayat 13 in Chichewa

42:13 Surah Ash-Shura ayat 13 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 13 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿۞ شَرَعَ لَكُم مِّنَ ٱلدِّينِ مَا وَصَّىٰ بِهِۦ نُوحٗا وَٱلَّذِيٓ أَوۡحَيۡنَآ إِلَيۡكَ وَمَا وَصَّيۡنَا بِهِۦٓ إِبۡرَٰهِيمَ وَمُوسَىٰ وَعِيسَىٰٓۖ أَنۡ أَقِيمُواْ ٱلدِّينَ وَلَا تَتَفَرَّقُواْ فِيهِۚ كَبُرَ عَلَى ٱلۡمُشۡرِكِينَ مَا تَدۡعُوهُمۡ إِلَيۡهِۚ ٱللَّهُ يَجۡتَبِيٓ إِلَيۡهِ مَن يَشَآءُ وَيَهۡدِيٓ إِلَيۡهِ مَن يُنِيبُ ﴾
[الشُّوري: 13]

Iye wakukhazikitsirani chipembedzo chimene adakhazikitsira Nowa kuti atsatire, ndi chimene tavumbulutsa kwa iwe, ndi chimene tidakhazikitsira Abrahamu ndi Mose ndi Yesu powauza kuti inu mukhazikitse chipembedzo ndipo musapatukane. Ndi kovuta kuti anthu osakhulupirira atsatire zimene iwe uwaitanira. Mulungu amasankha yekha onse amene wawafuna ndipo amatsogolera onse amene amagonja kwa Iye

❮ Previous Next ❯

ترجمة: شرع لكم من الدين ما وصى به نوحا والذي أوحينا إليك وما, باللغة نيانجا

﴿شرع لكم من الدين ما وصى به نوحا والذي أوحينا إليك وما﴾ [الشُّوري: 13]

Khaled Ibrahim Betala
“Wakhazikitsa kwa inu chipembedzo chonga chomwe adam’langiza Nuh. Ndipo chimene takuvumbulutsira iwe ndi chimenenso tidavumbulutsira Ibrahim, Mûsa, ndi Isa (Yesu) kuti: Mulimbike chipembedzo (potsatira malamulo) ndikuti musalekane pa chipembedzo. Koma ndizovuta kwa opembedza mafano (kuvomera) zimene ukuwaitanira. Allah amadzisankhira amene wam’funa ndipo amamuongolera amene akutembenukira kwa Iye
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek