×

Imeneyi ndi nkhani yabwino imene Mulungu ali kuwauza akapolo ake amene amakhulupirira 42:23 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:23) ayat 23 in Chichewa

42:23 Surah Ash-Shura ayat 23 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 23 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿ذَٰلِكَ ٱلَّذِي يُبَشِّرُ ٱللَّهُ عِبَادَهُ ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِۗ قُل لَّآ أَسۡـَٔلُكُمۡ عَلَيۡهِ أَجۡرًا إِلَّا ٱلۡمَوَدَّةَ فِي ٱلۡقُرۡبَىٰۗ وَمَن يَقۡتَرِفۡ حَسَنَةٗ نَّزِدۡ لَهُۥ فِيهَا حُسۡنًاۚ إِنَّ ٱللَّهَ غَفُورٞ شَكُورٌ ﴾
[الشُّوري: 23]

Imeneyi ndi nkhani yabwino imene Mulungu ali kuwauza akapolo ake amene amakhulupirira ndipo amachita ntchito zabwino. Nena, “Ine sindili kukupemphani malipiro ayi kupatula kuti muzionetsa chikondi kwa ine chifukwa cha ubale wanga ndi inu.” Ndipo aliyense amene alandira chabwino, tidzamuonjezera zabwino zambiri mofanana ndi izo. Ndithudi Mulungu ndi wokhululukira ndi wokonzeka kulipira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ذلك الذي يبشر الله عباده الذين آمنوا وعملوا الصالحات قل لا أسألكم, باللغة نيانجا

﴿ذلك الذي يبشر الله عباده الذين آمنوا وعملوا الصالحات قل لا أسألكم﴾ [الشُّوري: 23]

Khaled Ibrahim Betala
“Umenewu ndi (ulemelero) umene Allah akuwasangalatsira akapolo Ake nkhani yabwino; amene akhulupirira ndi kuchita zabwino. Nena (iwe Mtumiki {s.a.w} kwa iwo): “Sindikupemphani malipiro (kapena chuma) pofikitsa uthenga (kwa inu), koma kuti musunge chikondi pachibale chimene chili pakati pathu. (Musandizunze kufikira ndifikitse kwa inu uthenga wa Mbuye wanga.)” Amene achita chabwino timuonjezera pachabwinocho ndithu Allah Ngokhululuka kwambiri, Ngolandira kuthokoza
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek