×

Kapena iwo akuti, “Iye wapeka yekha bodza lokhudza Mulungu?” Ngati Mulungu akadafuna 42:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:24) ayat 24 in Chichewa

42:24 Surah Ash-Shura ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 24 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿أَمۡ يَقُولُونَ ٱفۡتَرَىٰ عَلَى ٱللَّهِ كَذِبٗاۖ فَإِن يَشَإِ ٱللَّهُ يَخۡتِمۡ عَلَىٰ قَلۡبِكَۗ وَيَمۡحُ ٱللَّهُ ٱلۡبَٰطِلَ وَيُحِقُّ ٱلۡحَقَّ بِكَلِمَٰتِهِۦٓۚ إِنَّهُۥ عَلِيمُۢ بِذَاتِ ٱلصُّدُورِ ﴾
[الشُّوري: 24]

Kapena iwo akuti, “Iye wapeka yekha bodza lokhudza Mulungu?” Ngati Mulungu akadafuna akadatseka mtima wako. Ndipo Mulungu amafafaniza bodza ndi kukhazikitsa choonadi ndi mawu ake. Ndithudi Iye amadziwa zinsinsi zonse zimene zili m’mtima

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أم يقولون افترى على الله كذبا فإن يشأ الله يختم على قلبك, باللغة نيانجا

﴿أم يقولون افترى على الله كذبا فإن يشأ الله يختم على قلبك﴾ [الشُّوري: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Kapena akunena kuti: “Wampekera Allah bodza?”Allah akadafuna akadadinda mu mtima mwako (kuti usathe kunena chilichonse; koma kuti chilichonse chimene ukunena chikuchokera kwa Iye). Ndipo Allah amachotsa chabodza (shirik), ndi kuchilimbikitsa choona (Chisilamu), ndi mau Ake (amene adawavumbulutsa kwa Mneneri Wake). Ndithu Iye Ngodziwa (zobisika) za mmitima
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek